Mawu Akumapeto
^ 3. Zina mwa ndalama zimene anthu amapereka mwa kufuna kwawo timazigwiritsa ntchito pothandizira anthu omwe akumana ndi ngozi zadzidzidzi. (Machitidwe 11:27-30) Popeza anthu amene amagwira ntchitoyi ndi ongodzipereka, ndalama zimene anthu amaperekazi sizimakhala zolipirira anthu koma zimakhaladi zothandizira anthu amene akhudzidwa ndi mavuto.