Mawu Akumapeto
^ [1] (ndime 12) Anthu ena amene anathetsa kusamvana mwamtendere ndi awa: Yakobo ndi Esau (Gen. 27:41-45; 33:1-11); Yosefe ndi abale ake (Gen. 45:1-15); ndiponso Gidiyoni ndi anthu a ku Efuraimu. (Ower. 8:1-3) Komanso mwina mukudziwa zitsanzo zina za m’Baibulo za nkhani ngati zimenezi.