Mawu a M'munsi
Tanthauzo la mawu achiheberi amene tawamasulira kuti “nyimbo yoimba polira” silikudziwika, koma mwina mawu amenewo angatanthauze nyimbo yoimba mokhudzidwa mtima kwambiri. Kaimbidwe kake kangasonyeze kuti moyo wa munthuyo uli pangozi, akufuula kupempha thandizo, kapena akukondwera ndipo akutamanda winawake.