Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

Mawu ake enieni, “kulemera.” Mawu achiheberi otanthauza “katundu wolemetsa” ali ndi matanthauzo awiri. Panopa m’lembali akutanthauza uthenga wamphamvu wochokera kwa Mulungu, koma pamalo otsatira m’lemba lomweli akutanthauza kuti anthuwo anali katundu wolemetsa kwa Mulungu. Choncho poyankha, Yeremiya anagwiritsa ntchito mawuwa chifukwa cha matanthauzo ake awiriwa.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena