Mawu a M'munsi
Tanthauzo la mawu achiheberi amene tawamasulira kuti “nyimbo yoimba polira” silikudziwika, koma mwina angatanthauze nyimbo yoimba mokhudzika mtima kwambiri. Kaimbidwe kake kangasonyeze kuti moyo wa munthu woimbayo uli pangozi, akufuula kupempha thandizo, kapena akukondwera ndiponso kutamanda winawake.