Mawu a M'munsi
Mawu ake enieni, “anaganiza zothetsa ukwati mwamseri.” Pa mwambo wachiyuda, kuti lonjezo loti anthu adzakwatirana lithe ankatsatira dongosolo lothetsera ukwati.
Mawu ake enieni, “anaganiza zothetsa ukwati mwamseri.” Pa mwambo wachiyuda, kuti lonjezo loti anthu adzakwatirana lithe ankatsatira dongosolo lothetsera ukwati.