Mawu a M'munsi
Pavesili m’mipukutu ina yachigiriki pali mawu akuti, “Kukoma mtima kwakukulu kwa Ambuye wathu Yesu Khristu kukhale ndi inu nonse. Ame.” Mawu amenewa akufanana ndi amene ali mu vesi 20. Koma mawuwa sapezeka m’mipukutu yakale kwambiri yachigiriki.