Mawu a M'munsi
a Kaamba ka umboni wakuti Ufumu wa Mulungu unakhazikitsidwa mu 1914 ndikuti dziko lino lakhala m’masiku ake otsiriza chiyambire nthaŵiyo, onani mitu 16 ndi 18 ya bukhu lakuti Mungathe Kukhala ndi Moyo Kosatha m’Paradaiso pa Dziko Lapansi, lofalitsidwa mu 1984 ndi Watchtower Bible and Tract Society of New York, Inc.