Mawu a M'munsi
a Popeza kuti unyinji wa makolo omwe ali okha ndiakazi, tidzagwiritsira ntchito mawu otchula munthu achikazi. Komabe, malamulo amakhalidwe abwino ofotokozedwa munomu amagwira ntchito kwa makolo omwe ali okha ponse paŵiri ŵamuna ndi ŵakazi.