Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

a Zikumbukiro zina zimayamba kubwera mwamtundu wa kuvutika malingaliro; zina zimakhala mwamtundu wa kubwebweta kumene kungatengedwe molakwa kukhala zochita za ziŵanda—phokoso losadziŵika, monga ngati kutseguka kwa zitseko; kuwona zideludelu za zinthu zomadutsa pa makomo ndi pa mazenera; kumva monga wagona ndi munthu m’kama. Kupsinjako kaŵirikaŵiri kumachepa pamene zikumbukiro zibwera bwino lomwe.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena