Mawu a M'munsi
b Chidziŵitso chothandiza minkhole ya kuchitiridwa nkhanza chimapezedwa pa masamba 25-30 m’kope la April 1, 1984, la magazini inzake ya ino, Nsanja ya Olonda. Tikulimbikitsa akulu ampingo onse kuwona m’kope lakale limeneli ndi kupereka chisamaliro chachikulu ku mbali zirizonse zowakhudza.