Mawu a M'munsi
c Kufufuza kunasonyeza kuti kuyerekezera zakugonana kaŵirikaŵiri kumakhala mbali yaing’ono kwambiri poyerekeza ndi malingaliro a zenizeni a munthu. Koma buku lakuti Daydreaming, lolembedwa ndi Dr. Eric Klinger limanena kuti: “Timakumbukira bwino kwambiri zinthu zimene zimadzutsa malingaliro athu. Koma kuyerekezera zakugonana kumadzutsa malingaliro kwambiri, mwinamwake timazikumbukira kwambiri kuposa zina zilizonse.”