Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

b Yesu ananenadi kwa otsutsana naye kuti: “Pasulani kachisi uyu, ndipo masiku atatu ndidzamuutsa.” (Yohane 2:19-22) Koma monga momwe Yohane akusonyezera, Yesu sanali kunena za kachisi wa mu Yerusalemu, koma za “kachisi wa thupi lake.” Motero Yesu anali kuyerekezera imfa yake yoyembekezeredwayo ndi chiukiriro, ndi kupasulidwa ndi kumangidwanso kwa nyumbayo.—Yerekezerani ndi Mateyu 16:21.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena