Mawu a M'munsi
b Yesu ananenadi kwa otsutsana naye kuti: “Pasulani kachisi uyu, ndipo masiku atatu ndidzamuutsa.” (Yohane 2:19-22) Koma monga momwe Yohane akusonyezera, Yesu sanali kunena za kachisi wa mu Yerusalemu, koma za “kachisi wa thupi lake.” Motero Yesu anali kuyerekezera imfa yake yoyembekezeredwayo ndi chiukiriro, ndi kupasulidwa ndi kumangidwanso kwa nyumbayo.—Yerekezerani ndi Mateyu 16:21.