Mawu a M'munsi
a M’Malemba onse, Yehova Mulungu amanena ponena za iyemwini kuti amada maganizo ndi makhalidwe auchimo. (Deuteronomo 16:22; Miyambo 6:16-19; 8:13; Yesaya 1:14; 61:8) Polingalira zimenezi, kusudzula konenedwa pa Malaki 2:16 kuyeneranso kukhala kwa mtundu wauchimo pamaso pake.