Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

a Kodi nchiyani chimene munthu amene akudziŵa kuti ali ndi AIDS ayenera kuchita pamene akufuna kukhala mmodzi wa Mboni za Yehova ndi kubatizidwa? Chifukwa cha kulemekeza malingaliro a ena, kungakhale kwabwino kwa iwo kupempha ubatizo wamtseri, ngakhale kuti palibe umboni wakuti AIDS yapatsiridwa kwa munthu kupyolera m’dziwe losambira. Pamene kuli kwakuti Akristu ambiri a m’zaka za zana loyamba anabatizidwa pa masonkhano aakulu apoyera, ena anabatizidwa mwamtseri chifukwa cha mikhalidwe yosiyanasiyana. (Mac. 2:38-41; 8:34-38; 9:17, 18) Njira ina ingakhale yakuti woyembekezera ubatizo wodwala AIDS abatizidwe pomaliza.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena