Mawu a M'munsi
c Kumbali zina za dziko, zisonyezero zapoyera za chikondi pakati pa anthu osakwatirana zimalingaliridwa kukhala zosayenera ndi zokhumudwitsa. Akristu amasamala kusadzisungira mwanjira ina iliyonse imene ingakhumudwitse ena.—2 Akorinto 6:3.