Mawu a M'munsi
a Kumbali ina, mlembi Alvin Rosenbaum akukumbutsa achichepere kuti: “Malingaliro a zakugonana ndi mikhalidwe ya maganizo zimasiyana kwambiri. Anthu ena amaoneka ngati sangaleke kulingalira za kugonana pamene ena samalingalira konse za kugonana. . . . Kachitidwe konseko nkachibadwa.” Iye akuwonjezera kuti: “Munthu aliyense amakula pa liŵiro losiyana.”