Mawu a M'munsi
b Mawu akuti “yomanga mofulumira” amanena za njira yolinganizidwa bwino koposa ya kumanga yoyambitsidwa ndi Mboni za Yehova. Antchito odzifunira amene amagwira ntchito imeneyi samalipidwa; amapereka mwaufulu nthaŵi yawo ndi nyonga. Chaka chilichonse pafupifupi Nyumba Zaufumu zatsopano 200 zimamangidwa ku United States, zinanso 200 zimakonzedwanso mwa kugwiritsira ntchito njira imeneyi.