Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

a Mu 1844, mtsogoleri wachipembedzo Wachibritishi, E. B. Elliott, anasumika maganizo pa 1914 kukhala deti lothekera la mapeto a “nthaŵi zisanu ndi ziŵiri” za m’Danieli chaputala 4. Mu 1849, Robert Seeley, wa ku London, analongosola nkhaniyo mofananamo. Joseph Seiss, wa ku United States, anasonyeza 1914 kukhala deti lofunika kwambiri m’kuŵerengera zaka kwa Baibulo m’chofalitsidwa chokonzedwa pafupifupi mu 1870. Mu 1875, Nelson H. Barbour analemba m’magazini ake a Herald of the Morning kuti 1914 inali mapeto a nyengo imene Yesu anatcha “nthaŵi zawo za anthu akunja.”—Luka 21:24.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena