Mawu a M'munsi
b Kuukira ndi mawu kungakhale mlatho wa ku ndewu ya m’banja. (Yerekezerani ndi Eksodo 21:18.) Phungu wina wa akazi omenyedwa akunena kuti: “Mkazi aliyense amene amafika kudzapeza lamulo lomtetezera pa kumenyedwa, kubayidwa, kapena kukhamidwa koika moyo wake pangozi, kuwonjezera pa zimenezi, wakhalapo ndi mbiri yaitali ya kuchitiridwa nkhanza mwamawu.”