Mawu a M'munsi
a Wotchi yoonera chiwonongeko cha dziko imene ili pa chikuto cha magazini ya The Bulletin of the Atomic Scientists ndi chizindikiro cha mmene anthu akuganizira kuti dziko layandikira “pakati pausiku” pa nkhondo ya nyukiliya. Kwa zaka makumi angapo m’mbuyomu, muvi wosonyeza mphindi wa wotchiyi wakhala ukusunthidwa kusonyeza mmene ndale zilili padziko.