Mawu a M'munsi
c Mboni za Yehova zili ndi thandizo la akulu a mpingo. Pamene kuli kwakuti saloŵerera nkhani za m’mabanja a eni, akuluwo angakhale othandiza komanso otsitsimula kwa mabanja amene ali pamavuto.—Yakobo 5:14, 15.
c Mboni za Yehova zili ndi thandizo la akulu a mpingo. Pamene kuli kwakuti saloŵerera nkhani za m’mabanja a eni, akuluwo angakhale othandiza komanso otsitsimula kwa mabanja amene ali pamavuto.—Yakobo 5:14, 15.