Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

a Ngati m’dziko lanu anthu ambiri amagwiritsa ntchito chinsalu pozimira moto, onetsetsani kuti mumadziŵa kuchigwiritsa ntchito bwino. Bungwe la U.S. National Fire Protection Association linati: “Tikufuna kugogomeza kuti . . . nsalu zozimira moto n’zongogwirizira basi. Ziyenera kugwiritsidwa ntchito kokha ngati zilipo pafupi. . . . Kusagwiritsa ntchito bwino nsalu zozimira moto kungawonjezere utsi ndiponso kuvulala ndi moto ngati chinsalucho chitakhotetsera utsi kumaso kwa munthu kapena ngati chitapanda kuchotsedwa malaŵi akazima.”

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena