Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

b Magazini yotchedwa New Scientist inanena kuti mbewu za ku Ulaya za sugar beet zimene “anazisintha chilengedwe chake kuti zisamafe ndi mankhwala ophera udzu m’munda zasinthanso pazokha kuti zisamafe ndi mankhwala amtundu winanso.” Mbewuzi zinasintha pamene zinalandira ufa wochokera ku mtundu wina wa mbewuzi umene unazisintha kuti zisamafe ndi mankhwala ena ophera udzu m’munda. Asayansi ena akuda nkhaŵa kuti n’kutheka kuti kugwiritsa ntchito kwambiri mbewu zotere kungapangitse kuti pakhale mtundu wa tchire la m’munda losamva mankhwala.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena