Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

f Madokotala amati ndi bwino kuti anthu odwala matendaŵa aziyenda ndi khadi lowadziŵikitsa ndi kutinso azivala zinthu monga zibangili kapena mphete, zosonyeza kuti ali ndi matendaŵa. Zinthu zikafika poipa zimenezi zingathe kum’pulumutsa wodwalayo. Mwachitsanzo, madokotala angathe kusokonezeka n’kuchepa kwa shuga m’magazi n’kumaganiza kuti ndi matenda ena mwinanso kuti ndi uchidakwa.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena