Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

a Si timadzi tokhati timene timawononga mwana yemwe ali m’mimba mwa amayi ake. Palinso fodya, mowa, ndi mankhwala ozunguza bongo omwe angachite chimodzimodzi. Ndi bwino kuti azimayi oyembekezera azipewa chilichonse chowononga. Komanso, ndi bwino kwambiri kufunsa dokotala kuti mudziŵe ngati mankhwala opatsa mayi woyembekezera angakhale oopsa kwa mwana yemwe ali m’mimba mwake.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena