Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

d Buku lakuti Israel in Egypt limati: “Zakuti Mose analeredwera m’nyumba yachifumu ya Aaigupto zimamveka ngati nthano chabe. Komano mukaonetsetsa mmene zinthu zinkayendera m’nyumba yachifumu ku Aigupto m’zaka za m’ma 1550 mpaka 1070 Nyengo Yathu Ino Isanakwane mungathe kuona kuti sinthano chabe ayi. Thutmose Wachitatu . . . anayambitsa zomatenga akalonga ogwidwa pankhondo ochokera m’mayiko a kumadzulo kwa Asia n’kuwapititsa ku Aiguptoko kuti awaphunzitse moyo wa Aaigupto . . . Motero, sizinali zachilendo kuona akalonga aamuna ndiponso aakazi ochokera kunja ali m’nyumba yachifumu ya ku Aigupto.”

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena