Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

a Buku lomwelo linati mosiyana ndi wachinyamata amene amasungulumwa nthawi zina, achinyamata ena amakhala osungulumwa nthawi zambiri ndiponso kwa nthawi yaitali. Wachinyamata woteroyo “amakhulupirira kuti adzakhala wopanda mnzake mpaka kalekale, kuti palibe chomwe angachite kuti asinthe zimenezo, ndiponso kuti zimenezi zili choncho chifukwa choti iyeyo ali ndi vuto.” Amakhulupiriranso kuti zinthu “sizingasinthe, kapena sizidzasintha.”

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena