Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

c Mboni za Yehova zapeza kuti buku lofotokoza za m’Baibulo lakuti Mafunso Achichepere Akufunsa—Mayankho Amene Amathandiza n’lothandiza kwambiri. Mutu uliwonse mwa mitu yake 39 umayankha funso lochititsa chidwi. Nayi mitu yake ina: “Kodi Ndingapange Bwanji Mabwenzi Enieni?” “Kodi Ndingalake Motani Chitsenderezo cha Ausinkhu Wanga?” “Kodi Ndingachititse Motani Kusukidwa Kwanga Kuchoka?” “Kodi Ndili Wokonzekera Kupalana Ubwenzi?” “Kodi Nkuneneranji Kuti Ayi ku Mankhwala Oledzeretsa?” “Bwanji Ponena za Kugonana Ukwati Usanachitike?”

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena