Mawu a M'munsi
a Mawu a Chigiriki amene anawamasulira kuti “dama” akuphatikizapo zachiwerewere zilizonse zomwe munthu wachita ndi munthu yemwe sanakwatirane naye zimene zimaphatikizapo kugwiritsa ntchito maliseche, monga kugonana m’kamwa.—Onani Galamukani! ya August 8, 2004, tsamba 12, ndi Nsanja ya Olonda ya February 15, 2004, tsamba 13, yofalitsidwa ndi Mboni za Yehova.