Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

b Akuluakulu ena amagona ana pofuna kukhutiritsa zilakolako zawo. Iwo kawirikawiri amachita zimene Baibulo limazitcha dama, kapena kuti por·neiʹa, zomwe zimaphatikizapo kuchita zinthu monga kuwaseweretsa maliseche, kuwagona, ndiponso kuwagona m’kamwa kapena kumatako. Zina mwa nkhanza zomwe akuluakulu amachita kwa ana ndi kuwasisita mabere, kuwanyengerera kuti achite nawo zopusa, kuwaonetsa zinthunzi zolaula, kuwaonera, ndiponso kuwaonetsa maliseche. Baibulo limaletsa zimenezi ndipo limazitcha ‘khalidwe lotayirira, lonyansa kapena ladyera.’—Agalatiya 5:19-21; Aefeso 4:19.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena