Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

a Akatswiri ankhaniyi amanena kuti ngakhale kuti ana ambiri amene anachitidwapo chipongwe choterechi saulula, amachita zinthu zoonetsa kuti zinazake sizili bwino. Mwachitsanzo, mukaona mwana atayambanso mosadziwika bwino kuchita zizolowezi zimene anasiya kale, monga kukodza pamphasa, kusafuna kusiyana nanu, kapena kuopa kukhala yekha, dziwani kuti kalipokalipo. Koma sikuti mukangoona zimenezi basi ndiye kuti mwana wanu anachitidwa zachipongwe. Mufunseni mwana wanu modekha kuti akufotokozereni zimene zikumuvutitsa maganizo kuti muthe kumulimbikitsa, ndi kum’teteza bwinobwino.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena