Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

a Ndi bwino kusamala mukamagwira mbalame imene yavulala, chifukwa iyoyo siidziwa kuti mukufuna kuithandiza. Komanso pali mbalame zina zimene zimakhala ndi matenda amene angagwirenso anthu. Motero ngati mukufuna kuthandiza mbalame yovulala, ndi bwino kuvala magulovu ndipo muzisamba m’manja mukamaliza. Ngati mukuona kuti mbalameyo ingathe kukuvulazani, musaiyandikire. Mungathenso kuitana akatswiri a zachilengedwe, ngati pangafunike kutero.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena