Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

a Mfundo imeneyi anayambitsa ndi katswiri wina wazachuma wa ku Italy, dzina lake Vilfredo Pareto. Iye ananena kuti nthawi zambiri tingagwire chintchito chachikulu m’kanthawi kochepa. Mfundo imeneyi imagwira ntchito pa zinthu zosiyanasiyana. Mwachitsanzo, mukamayeretsa m’nyumba, fumbi lambiri limachokera malo amene anthu amakonda kudutsa ndipo malo amenewa amakhala aang’ono kwambiri. Choncho, kungosesa malo amenewo mumakhala kuti mwagwira ntchito yaikulu kuposa kuwononga nthawi kusesa malo akulu omwe sanade kwenikweni.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena