Mawu a M'munsi
b Nthawi zambiri kachipangizoka kamakhala ndi kagudumu komwe kamazungulira mofulumira pakachitsulo kena. Kagudumuka sikasiya kuzungulira ngakhale mutamakasunthasuntha kapena kukazondotsa. N’chifukwa chake kachipangizo kameneka kamagwiritsidwanso ntchito kupangira makampasi.