Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

b Baibulo limaphunzitsa kuti munthu akafa amangokhala ngati wagona, ndipo amangoyembekezera kuti adzaukitsidwe. (Mlaliki 9:5; Yohane 11:11-14; Machitidwe 24:15) Koma zimene anthu amakhulupirira kuti munthu amakhala ndi chinachake chomwe sichifa munthuyo akamwalira n’zosamveka chifukwa ngati pali chinachake chomwe sichifa, ndiye kuti palibe chifukwa choti akufa adzaukitsidwe.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena