Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

a Ena akutchula chifukwa china chakuti: Ayuda angakhale atasonkhezeredwa ndi nthanthi Yachigiriki. Mwachitsanzo, Philo, wanthanthi Wachiyuda wa ku Alexandria amene anali kukhala ndi moyo pafupifupi m’nthawi ya Yesu, anasonkhezeredwa kwakukulu ndi wanthanthi Wachigiriki Plato, amene anamlingalira kuti anauziridwa ndi Mulungu. Lexikon des Judentums (Dikshonale ya Chiyuda), pamutu wakuti “Philo,” imalongosola kuti Philo “anagwirizanitsa chinenero ndi ziganizo zanthanthi Yachigiriki (Plato) limodzi ndi chikhulupiriro chovumbulutsidwa cha Ayuda” ndi kuti poyambirira “anali ndi chiyambukiro chowoneka pa abambo atchalitchi Chachikristu.” Philo anaphunzitsa kuti Mulungu anali wosakhoza kulongosoledwa ndipo, chifukwa cha chimenecho, anali wopanda dzina.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena