Mawu a M'munsi
c Chifukwa cha chimenecho olemba mabukhu ena otanthauzira mawu amazindikira ‘oh·lamʹ monga momwe lagwiritsiridwira ntchito pa Mlaliki 1:4 kukhala likutanthauza “kosatha.” The New English Bible, Revised Standard Version, The Jerusalem Bible, The Bible in Living English, King James Version ndipo ena amatembenuza m’njira imeneyo.