Mawu a M'munsi
a Munthu wina wachiroma wolemba mbiri dzina lake Tacitus analemba kuti adani atalanda mzinda wa Yerusalemu mu 63 B.C.E., Cneius Pompeius analowa m’nyumba yopatulika ya pakachisi koma sanapezemo chilichonse. M’kachisimo munalibe likasa la pangano.—Tacitus History, 5.9.