Mawu a M'munsi
b Dzina lakuti “Belitsazara” limatanthauza kuti “Tetezani Moyo wa Mfumu.” “Sadrake” lingatanthauze kuti “Lamulo la Aku,” mulungu wa mwezi wachisumeriya. “Mesaki” kukhala ngati limanena za mulungu wachisumeriya, ndipo “Abedinego” limatanthauza “Mtumiki wa Nego,” kapena Nebo.