Mawu a M'munsi
a Malinga ndi zimene ananena Myuda wina wolemba mbiri yakale dzina lake Josephus, “magaleta 600, amuna 50,000 okwera pamahatchi komanso chigulu cha asilikali oyenda pansi okwana 200,000 ndi amene ankalondola” Aheberi.—Jewish Antiquities, II, 324 [xv, 3].