Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

a “Nthawi yobwezeretsa zinthu zonse” inayamba pamene Ufumu wa Mesiya unakhazikitsidwa komanso pamene mbadwa ya Mfumu Davide, yemwe anali wokhulupirika, inakhala Mfumu. Yehova analonjeza Davide kuti mmodzi wa mbadwa zake adzalamulira mpaka kalekale. (Salimo 89:35-37) Koma Ababulo atawononga Yerusalemu mu 607 B.C.E., palibe mbadwa ya Davide iliyonse imene inakhala pampando wachifumu wa Mulungu. Yesu, amene anabadwa monga wolowa ufumu wa Davide, anakhala Mfumu yomwe Mulungu analonjeza kalekale, pamene anapatsidwa Ufumu kumwamba.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena