Mawu a M'munsi
a Mawu a Chiheberi omwe anawamasulira kuti “ndodo” ankatanthauza kamtengo kamene m’busa ankagwiritsa ntchito poweta nkhosa. (Salimo 23:4) Mofanana ndi zimenezi, mfundo yakuti makolo ayenera kugwiritsa ntchito “ndodo” polangiza ana awo ikusonyeza kuti ayenera kuchita zimenezi mwachikondi, osati mwankhanza.