Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

a Ponena za Yobu, Yehova anati: “Padziko lapansi palibe wina wofanana naye.” (Yobu 1:8) Ndiye kuti Yobu anakhalako Yosefe atamwalira kale komanso Mose asanasankhidwe kukhala mtsogoleri wa Aisiraeli. Choncho zinali zolondola pa nthawiyo kunena kuti panalibe yemwe anali wokhulupirika ngati Yobu.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena