Mawu a M'munsi
a Kale, makalipentala ankamanga nyumba, kupanga zinthu zamatabwa ndiponso kupanga zipangizo zaulimi. Justin Martyr, wa zaka za m’ma 100 C.E., analemba zokhudza Yesu kuti: “Ali padzikoli ankagwira ntchito ya ukalipentala ndipo ankapanga mapulawo ndi magoli.”