Mawu a M'munsi
b M’Baibulo muli mawu ena omwe analembedwa mofanana ndi amenewa. Mwachitsanzo, timawerenga kuti “Mulungu ndiye kuwala” ndiponso kuti “Mulungu . . . ndi moto wowononga.” (1 Yohane 1:5; Deuteronomo 4:24) Koma mawuwa tiyenera kuwaona kuti ndi ophiphiritsa chifukwa akuyerekezera Yehova ndi zinthu zooneka. Yehova ali ngati kuwala, chifukwa ndi woyera ndiponso wolungama. Kwa iye kulibe “mdima,” kapena kuti chinthu chodetsedwa. Ndipo tingamuyerekezere ndi moto chifukwa amagwiritsa ntchito mphamvu zake zowononga.