Mawu a M'munsi
a Katswiri wina wa Baibulo anati kufiira kotchulidwa palembali sikunkasuluka ngakhale pang’ono. Chinthu chamtunduwu sichinkasintha maonekedwe ngakhale atachiika pamame, pamvula, kuchichapa kapena kuchigwiritsa ntchito kwa nthawi yaitali.