Mawu a M'munsi
b N’chifukwa chake Baibulo limagwirizanitsa choonadi ndi kuwala. Wolemba masalimo anaimba kuti: “Tumizani kuwala kwanu ndi choonadi chanu.” (Salimo 43:3) Yehova amapereka kuwala kwakukulu kwauzimu kwa anthu amene amafuna kuti iye awaunikire, kapena kuti awaphunzitse.—2 Akorinto 4:6; 1 Yohane 1:5.