Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

a Malamulo a Arabi ankanena kuti munthu azitalikirana ndi wakhate pafupifupi mamita awiri. Ndipo ngati kukuwomba mphepo, wakhate ankafunika kutalikirana ndi anthu pafupifupi mamita 45. Buku lina limanena za Rabi wina yemwe ankabisala akaona akhate ndiponso wina amene ankawathamangitsa powagenda ndi miyala. (Midrash Rabbah) Choncho anthu akhate ankadziwa mmene zimapwetekera ukamakanidwa, kunyozedwa komanso kuona kuti anthu sakukufuna.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena