Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

b M’mipukutu ina yakale, mulibe mawu oyambirirawa apalemba la Luka 23:34. Koma chifukwa chakuti mawuwa amapezeka m’mipukutu ina yambiri yodalirika, anaikidwa mu Baibulo la Dziko Latsopano komanso m’Mabaibulo ena ambiri. Yesu ayenera kuti ankanena za asilikali a Chiroma amene anamupachika. Iwo sankadziwa zimene ankachita chifukwa sankadziwa kuti Yesu anali ndani. Mwinanso Yesu ankaganizira za Ayuda omwe anapempha kuti iye aphedwe koma patapita nthawi anayamba kumukhulupirira. (Machitidwe 2:36-38) Koma atsogoleri achipembedzo amene anachititsa kuti Yesu aphedwe, anali ndi mlandu waukulu chifukwa ankadziwa zimene akuchita ndipo anachita zimenezo chifukwa chongodana naye. Ambiri mwa anthu amenewa sanakhululukidwe.​—Yohane 11:45-53.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena